Choyamba ndikuthokoza Mulungu bwana Wazolengedwa zonse. Mtendere ndi madalistso a Mulungu akhale kwa Mtsogoleri wa Aneneri onse, Mtumiki Wathu Muhammadi pamodzi ndi akubanja kwake, Ophunzira ake ndi omutsatira Onse. Ndikuyikira Umboni kuti palibe Mulungu Wina Koma Mulungu Mmodzi Yekha, Komanso Muhammadi (Mtendere ndi Madalitso a Mulungu a Khale Kwaiye) Ndi Mthenga Wake, Zonsezi Potsimikidza ndi Mtima, Kulankhula ndi lilime Komanso Kugwiritsa ntchito thupi potsatira Malamulo ache.
gawani: